Ulemelero wa Imam Husein (A.S) Part-1

Mngelo Jibril adafika kwa mtumiki (s.a.a.w) ndipo adamusangalatsa mtumiki Muhammad (s.a.a.w) pomuwuza kuti posachedwapa mwana wako wamkazi Fatima (a.s) azakhala ndi mwana yemwe adzaphedwa ndi Ummah wako pambuyo pako.

AttachmentSize
File b9da686f81518f5c62cbc64bcf4e8cc3.mp429.4 MB

Add new comment