Chilungamo ndi chiti? Part-3

Mulungu adamupatsa munthu mboni ziwiri kapena kuti atumiki awiri, Mtumiki ndi nzeru. Cholinga chomwe Mulungu adalengera zinthu ziwirizi ndi chimodzi komwe kuli kuwawongolera anthu ku chilungamo. Mwachoncho ndi zachidziwikire kuti ngakhale ndi pang’ono pomwe zinthu ziwirizi sizidzatsutsana ndipo sizingatheke kuti zitsutsane mpakana kalekale.

AttachmentSize
File f7c9bfa0240a21a29d7ee2735a59c562.mp419.69 MB

Add new comment