Kodi Quran idasokonezedwa kapena ayi? (1)

Kodi kunena kuti Bismillahi yemwe akupezeka kumayambiliro kwa Sura sigawo la Quran, sindiko kukhulupilira kuti mu Quran muli zinthu zina zomwe zidangolembedwa ndi anthu ndipo sizochokera kwa Mulungu?

AttachmentSize
File 63506ad3cc7ff121cfbd23f85cc63dcd.mp445.08 MB

Add new comment