Kodi Quran idasokonezedwa kapena ayi? (2)

Choti mudziwe abale athu okondedwa, nkhani iri apa siyofuna kuwanena ma Shia kuti amakhulupilira za Quran ina ayi. Ndithudi anthu omwe amaterowo amadziwa bwino lomwe kuti Shia samakhulupilira za kusokonezeka kwa Quran ayi komanso samagwadira Ahalbait (A.S) ndinso samawafikitsa pa mlingo wa Umulungu

AttachmentSize
File c53b6b74ee784ae3e658a7621b437147.mp421.53 MB

Add new comment