Kodi Quran idasokonezedwa kapena ayi? (3)

Choti mudziwe abale athu okondedwa, nkhani iri apa siyofuna kuwanena ma Shia kuti amakhulupilira za Quran ina ayi. Ndithudi anthu omwe amaterowo amadziwa bwino lomwe kuti Shia samakhulupilira za kusokonezeka kwa Quran ayi komanso samagwadira Ahalbait (A.S) ndinso samawafikitsa pa mlingo wa Umulungu

AttachmentSize
File 1e98640d2d85ed17f917f25a624c8220.mp420.97 MB

Add new comment