Kodi tidzayankha chiyani mu usiku wathu oyamba m’manda: Imam (mtsogoleri) wathu ndi ndani?-2

Imam Ali (A.S) pankhondo ya Siffin adanena kuti: أنا النبأ العظیم الذی فی اختلفتم و فی خلافتی تنازعتم “Ine ndiye nkhani yaikulu ija yomwe inu mudasemphana komanso mudakangana pokhudzana ndi ulowa m’malo wanga

AttachmentSize
File 927f59d6ac883e0bd1dd4ec374d43fee.mp428.89 MB

Add new comment