Kodi Quran idasokonezedwa kapena ayi? (1)

Choti mudziwe abale athu okondedwa, nkhani iri apa siyofuna kuwanena ma Shia kuti amakhulupilira za Quran ina ayi. Ndithudi anthu omwe amaterowo amadziwa bwino lomwe kuti Shia samakhulupilira za kusokonezeka kwa Quran ayi komanso samagwadira Ahalbait (A.S) ndinso samawafikitsa pa mlingo wa Umulungu

AttachmentSize
File c1a42966b808511fbbc24af0c299cc35.mp421.53 MB

Add new comment