Utumiki:Gawo 25 (B)

Mipatuko iwiri imeneyi (Shia ndi Sunni) ndiofanana muzikhulupiriro zokhudza Mtumiki (s.a.w.w).
Onse amakhulupirira kuti Mtumiki ndi:
- otumizidwa ndi Mulungu.
- Mtumiki omaliza.
- Munthu osankhidwa ndi Mulungu kudzaongola anthu.

AttachmentSize
File 0cec7c7a642abbf7f6e9e8da2e6b54ae.mp429.2 MB

Add new comment