فیلم

IMAMU MAHADI A.S
NKHANI YAKULA UMUMU NDI YOLONGONSOLA UMTSOGILERI WATHU CHIPEMBEDZO CHACHISILAMU CHI NDITHU WA NTHAWI INOYO PAMBUYO POTI PADUNSA AZIMTSOGOLERI A MULUNGU OCHOKELA KU BANJA LA MTUMIKI MUHAMMADI S.A.W IKWANA 11 . NDIYE KUTI AMENE ALIPO NTHWI INOYO NDI OMALID
MLOLWA WA PAMBUYO PA MTUMIKI MUHAMMADI S.A.W.
UMU NKHANI YAKULA MU PHUDZILO LATHU LI NDI NKHANI YA MMLOWA MMALO WA AKUBANJA LA MTUMIKI NDITHU , NDITHU MONGA NGATI UKULONGONSOLA KUTI OYENELA KUKHALA MTSOGOLERI AKYENELA KUNKHIDWA NDI MULUNGU KAPENA NDI MTUMIKI MWINI WAKE NDITHU. PA UMBONI UWU اني جاعل
UMTSOGOLERI PA MBUYO PA MTUMIKI MUHAMMADI AKUYENERA KUKHALA NDANI
UMUMU TIKULONGONSOLELANA NKHANI YOKHUDZA MTSOGOLERI WA PAMBUYO PA MTUMIKI MUHAMMADI S.A.W … KOMANSO NDI UBWINO OKHALA NDI MTSOGOLERI MU DZIKO KAPENA MU MU SOCIETY NDITHU.
KUPEMPHELELA CHINA CHAKE  POSAKHALA MULUNGU  MMODZI  NDI KOLENSEDWA NDITHU  KAPENA KUTI  SHIRKI NDITHU.
NDITHUDI KUGWADILA PONSAKHALA ALLAH AMENE ALI MMODZI YEKHA NDI KULENSEDWA PA MANSO PA ALLAH NDITHU , KOMANSO ANGAKHALE KUPELEKA ULEMU KWAMBIRI KWA CHOLENGEDWA CHA MULUNGU NDIKULENDWANSO NDITHU .
KUNSACHIMWA  KWA AKUBANJA LA MTUMIKI MUHAMMADI S.A.W.
MPATUKO WA CHI JAFARI A.S UMAKHULUPILILA ZOTI AMTSOGOLERI A CHIPEMBEDZO KAPENA ( ALOWA MMOLOWA A MULUNGU ) SAKUYENELA KUKHALA OPANGA ZA MACHIMO NDITHU . CHIFUKWA AKAKHALA OCHIMWA PA MANSO PA GULU SAKHALA ANTHU AZINSADZO ZABWINO NDITHU
NDITHUDI KUGWADILA PONSAKHALA ALLAH AMENE ALI MMODZI YEKHA NDI KULENSEDWA PA MANSO PA ALLAH NDITHU , KOMANSO ANGAKHALE KUPELEKA ULEMU KWAMBIRI KWA CHOLENGEDWA CHA MULUNGU NDIKULENDWANSO NDITHU .
UMUMU TIKULONGONSOLELANA NKHANI YOKHUDZA MTSOGOLERI WA PAMBUYO PA MTUMIKI MUHAMMADI S.A.W … KOMANSO NDI UBWINO OKHALA NDI MTSOGOLERI MU DZIKO KAPENA MU MU SOCIETY NDITHU
MLOLWA WA PAMBUYO PA MTUMIKI MUHAMMADI S.A.W.
NKHANI YAKULA UMUMU NDI YOLONGONSOLA UMTSOGILERI WATHU CHIPEMBEDZO CHACHISILAMU CHI NDITHU WA NTHAWI INOYO PAMBUYO POTI PADUNSA AZIMTSOGOLERI A MULUNGU OCHOKELA KU BANJA LA MTUMIKI MUHAMMADI S.A.W IKWANA 11 . NDIYE KUTI AMENE ALIPO NTHWI INOYO NDI OMALID
Ndi udindo wanji pa nthawi imene Imamu Mahadi akadali mobinsikamu ????
Ndi udindo wa inu ndi ine ndi oti I mamu Mahadi akadali mobinsika mu ndi mudziwa koma pogwilinsila ntchito mtima ndithu osati mu thupi ndithu. Chabe ndithu , komanso kuonjedzelapo nkhani ina ndi yakuti udindo wina mwa ifeyo ndi oti ndithu . kumuthandidz
NANGA KODI MA SHIA ALIE A.S AMATENGA KUKHALA MULUNGU KODI NDI ZOONA ?
Mu nkhani iyi ikutifotojodzela ndithu nkhani yopanga duwa kudzela kwa anthu , okondedwa inalipo ndithu. Komanso Imamu sajjadi adalankhula pa nkhani ndidzovomeledza kupempha mu njila anthu amenewa olemekedza wa ndithu. Monga ngati olo abale ake a nabbi
chidule cha nkhani ya umumu ndi choti pa umtsogoleri wa pambuyo pa mtumiki muhammadi kuti kodi umtsogoleri akuyenela kusankha anthu or mtumiki mwini wake mtumiki yu ? umumu zikutanthaudzanso kuti azathu asunni amati umtsogoleri ndi nthambi chabe ya chis
ZANABU ANALI akuwalimbikinsa za kupilila Azi chimwene ake Hassani ndi Hussain A.s
cholinhga chomtumidza muhammadi s. a.w ndi kudzapulumunsa wa nthu ndithu. ku makhalidwa oipa ndithu. komanso mtumiki anali ndi zipangidzo zokwanila zozapulumunsila anthu ndithudi za umzimu ndithu. komanso anali odalilika ndithu , komanso anali wa chinsadz

Pages