Mitundu ya Ibadah (2)

Anthu ena akumugwadira Mulungu ndi cholinga chofuna mtendere wake omwe ali malonda, ena akumugwadira Mulungu chifukwa chowopa moto wa Mulungu, omwe ali mapemphero a akapolo ndipo ena akumugwadira Mulungu chifukwa chongomuthokoza, omwe ali mapemphero a amfulu….

AttachmentSize
File 515d4a929a06149a5c5a1c111cc2a980.mp415.34 MB

Add new comment