Mitundu ya Ibadah (1)

Anthu ena akumugwadira Mulungu ndi cholinga chofuna mtendere wake omwe ali malonda, ena akumugwadira Mulungu chifukwa chowopa moto wa Mulungu, omwe ali mapemphero a akapolo ndipo ena akumugwadira Mulungu chifukwa chongomuthokoza, omwe ali mapemphero a amfulu….

AttachmentSize
File 6d47e6a3e19f3dc06b062f896c92ab6d.mp422.72 MB

Add new comment