Ma Ayah olozera za Imam Mahdi (AJ)-2

Tikamawona mu Quran, tikupezamo kuti muli ma Ayah ena omwe uthenga wake mpakana pano siudachitike, kapena zomwe zanenedwazo sizidachitike. Zomenezi zidzachitika nthawi ya Imam Mahdi (AJ)

Add new comment