Tawassul 2

Hadithiyi ndiyoti munthu wina osaona adabwera kwa Mtumiki (s.a.w.w) ndikumupempha kuti ampempherere kuti akhale bwino, Mtumiki adamuwuza kuti achite udhu mosamala kenako apemphere marakat awiri kenako apemphe ndi pempho kenako adakhala bwino.

AttachmentSize
File f94473368b8e415f3173df324da380b8.mp421.89 MB

Add new comment