Wahabiyyat 2

Chiwahabi chidadzi ndi Muhammad bin Abdul Wahhabi, iyeyu adali ndi zikhulupiriro zodabwitsa kwambiri monga kunena kuti Mtumiki (s.a.w.w)  adali munthu ngati ine mwachoncho inenso nditha kupanga zofanana ndizomwe iye amapanga , ndithanso kukhala Mtumiki.

AttachmentSize
File 9407c4f8a1ca9c5e584fc97ada6bfb50.mp432.61 MB

Add new comment